NKHANI

Unduna waza umoyo wati uyamba kugawa ma net woteteza ku udzudzu m’boma la Salima

Wolemba Melie Chipula Bayani.

Unduna waza umoyo wati uyamba kugawa ma net woteteza ku udzudzu m’boma la Salima mu miyezi ya October komanso November mboma li.

Poyankhula pa mkumano wa atengambali ochokela ku Mthambi zosiyanasiyana m’boma a Salima, mkulu wowona za nthenda ya malungo pa chipatala cha Salima Cosmas Phiri wati kugawidwa kwa ma net wa kwadza kaamba ka kuchuluka kwa chiwelengero cha anthu odwala nthenda ya Malungo.

Tags
Show More

Related Articles

Back to top button
Close
Close